Chewa translation

Ayah by Ayah

Tags

Download Links

Chewa translation translation for Surah Al-Qalam — Ayah 18

68:18
وَلَا يَسۡتَثۡنُونَ ١٨
Ndipo sadapatule (ngakhale wosauka ndi m’modzi yemwe ponena kuti uje timpatse, uje tisampatse, kapena sadanene kuti: “Ngati Allah afuna).”