Chewa translation

Ayah by Ayah

Tags

Download Links

Chewa translation translation for Surah Al-Muzzammil — Ayah 7

73:7
إِنَّ لَكَ فِي ٱلنَّهَارِ سَبۡحٗا طَوِيلٗا ٧
Ndithu masana uli ndi zochitachita zambiri; (umatanganidwa ndi ntchito yauthenga; dzipatse danga usiku polimbika kupemphera).