Chewa translation

Ayah by Ayah

Tags

Download Links

Chewa translation translation for Surah Al-Mursalat — Ayah 11

77:11
وَإِذَا ٱلرُّسُلُ أُقِّتَتۡ ١١
Ndi pamene atumiki adzasonkhanitsidwa pa nthawi yake, (kuti apereke umboni ku mibadwo yawo).