Chewa translation

Ayah by Ayah

Tags

Download Links

Chewa translation translation for Surah As-Saffat — Ayah 12

37:12
بَلۡ عَجِبۡتَ وَيَسۡخَرُونَ ١٢
Koma iwe (Mneneri) ukudabwa (za kutsutsa kwawo kuuka ku imfa pomwe zisonyezo zilipo zambirimbiri), ndipo akukuchitira chipongwe (kudabwa kwako).